26.5 C
Blantyre
Thursday, June 1, 2023
- Advertisement -spot_img

CATEGORY

Nkhani Za MMaboma

Amenyedwa Ndi Mwana Kamba Kozemba

Anthu a m’mudzi wina mdera la Mfumu Mabulabo mboma la Mzimba anafa ndi phwete pamene mkulu wina anamenyedwa ndi mwana wachichepere chifukwa chozemba kubweza...

Ataya Zambili Pofuna Zambili

Mkulu wina ku Thondwe mboma la Zomba wapita ku Lilongwe asakufuna, mbili itamveka kuti wapereketsa ndalama yokwana 200 thousand kwacha chifukwa chofuna kulemera. Nkhaniyi ikuti...

Njoka Yokawa Igwidwa Ku Kasungu

Mkulu wina kwa Wimbe mboma la Kasungu wazunguzia mutu munthu wina yemwe sakudziwika atagwira njoka yake yokawa. Nkhaniyi ikuti mkuluyo ndi nkhalakale pa bizinesi koma...

Alodza Mwana Wake Kuti Asazakwatiwe Kamba Ka Umbombo

Mtsikana wina yemwe amagwila ntchito ya uphunzitsi pa sukulu ina ku Dwangwa m’boma la Nkhotakota akulila usiku ndi usana mai ake omubala atamuthetsela banja. Nkhani-yi...

Latest news

- Advertisement -spot_img